COCA COLA SUPPORTING 1 MILLION JOBS IN AFRICA
The Coca-Cola Company announced the results of a comprehensive, Africa-wide socio-economic impact study during the 2025 U.S.-Africa Business Summit in Luanda, Angola. The study shows that the Coca-Cola system, made up of The Coca-Cola Company and its authorized bottlers, working with a wide network of suppliers, manufacturers, service providers and customers, contributed $10.4 billion in […]

KUKONZEKERA KUKHALA NDI NDALAMA ZOKHAZIKIKA
Pa chirichonse chimene munthu amachita kukonzekera kumafunikira. Zinthu zikamachitidwa zosakonzekera zimaonekera ng’amba. Ndalama nayo kuti ikhazikike imafunika kuyikonzekera. Mphunzitsi wa maphunziro abwino a kayendetsedwe ka chuma kuchokera ku Old Mutual, Benard Chiluzi watsindika za kufunikira kokhala ndi Ndalama zokhazikika. “Pali anthu ena Ndalama sizimawavuta kupeza, pali anthu ena Ndalama zomwezi zimaathawa.Tikamakàmba za kukhala ndi Ndalama […]

NAIROBI CITY THUNDER CLINCH FIRST WIN, AL AHLI TRIPOLI STAYS PERFECT
Nairobi City Thunder (Kenya) notched their first victory in the 2025 BAL Nile Conference , pulling off a surprise 85-76 win over South Africa’s MBB in the opening game of Day 5. Albert Odero spearheaded Thunder’s effort with a team-high 23 points, while five other players also scored in double figures. Nairobi dominated the boards […]

MALAWI ASATAYE NTHAWI NDI ULIMI WA MAKOLO
Posachedwapa njala ikukodolerani ku zakudya zofuma ku Ulimi. Si Ulimi onse omwe umabweretsa zokolola zochuluka koma wa makono. Katswiri pa nkhani za chuma ndi ulimi, Dr. Felix Jumbe,wafotokoza kuti ulimi wa Makomo ndi Ulimi wa dongosolo,umene umapereka ndalama zokhala chuma cha dziko. “Tikamati dziko la Malawi ndi losawuka timanena inu pa Banja lanu, tikamatinso Malawi […]
