Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist

Kasupe News

Page: 3

Pa zinthu zomwe munthu amaganizira tsiku ndi tsiku ndalama  imakhala pa mndandanda wa zinthu zoganiziridwa. Kaganizidwe kangwiro nako ndi kofunikira pa nkhani ya ndalama. Benard  ChiluzI, yemwe ndi Mkulu oyang’ana za maphunziro abwino a kayendetsedwe ka chuma ,wati kuganiza molungama ndi kaganizidwe komwe sikungamupezetse munthu mavuto kapena ndi kuganiza mu njira ina chifukwa cha zinthu […]

Litsiro ndi chinthu chokhacho chimene tsiku lake lobadwa silimadziwika ndipo limaberekana mwa kathithi. Mthupi mwa munthu namo mumakhala litsiro. Namkungwi pa nkhani ya zakudya,  Gladys Bandawe ,kuchokera ku Hope nutrition Services, watutumutsa mtundu wa a Malawi ponena kuti mthupi mwa munthu mumakhala litsiro.” Mkati mwathupi mumakhala litsiro limene limafunika kutsuka chimodzimodzi   limene limakhala kunja kwa […]

Pa miringo ya zinthu zomwe zimalingidwa pali mulingo umodzi wokha umene umapereka mafunso   ngati kalingidwe kakusemba ndondomeko maka olingayo akakhala wa mamuna ndipo akulinga munthu wa mkazi. Chovala , ndi chithu chokhacho chomwe chimalingidwa ndi mmisiri wosoka. Thomson Geza, Yemwe ndi mmodzi mwa wosoka zovala ku msika wa  Galliver mu mzinda wa Lilongwe, wavomereza kuti […]

Kusowa kwa maphunziro a za Chuma  pakati pa a Malawi  kuli ngati kusowa kwa  Chipatso cha Mpinjipinji Mnkhalango za dziko lino.Katswiri pa nkhani za Chuma a Innocent Banda, watsindika kuti ma Phunziro a za Chuma ndi osowa ngakhale ali ofunika. “Maphunziro a za chuma ndi ofunika chifukwa ndi chimene chimapereka mphamvu kwa anthu pothetsa umphawi,kutukula […]

Ndizosabisa kunena kuti Moto wa khala la Mtengo wa Tsanya omwe umayaka ku Bungwe lothana ndi Katangale ndi Ziphuphu  tsopano uli ngati Moto wa Mapesi. Katswiri woyankhulapo pa nkhani za Utsogoleri wabwino komanso momwe zinthu zikuyendera mdziko muno   Victor  Chipofya, wati sakumva nkhani  mma Nyuzipepala  ngati momwe zinaliri mbuyomu .”Sitikumva zinthu mma Nyuzipepala ngati mmene […]

Mdima wa ndiwe yani  wokhudza zomwe zidachitika kuti ndege yomwe idanyamula wachiwiri wa kale wa  Mtsogoleri wa dziko lino Malemu Dr Saulosi Klaus Chilima , udakakodolabe Mitsinje ya misonzi kwa a Mary Chilima ,omwe  pa 29 September 2024  adalemba pa tsamba la mchezo la facebook  kupempha  okhuzidwa onse kuti awathandize kupanga kafukufuku wapadera. Iwo adajambulitsa  […]

Mkuluwiko wokuti zingalume phula n’tenga ndi nkuluwiko omwe wamangirira  uthenga omwe Mtsogoleri wa dziko lino  Dr Lazalus Chakwera,  anali nawo kwa mamulumuzana a Bungwe la mgwirizano wa Maiko  apa dziko lonse lapansi. Mmodzi mwa akatswiri omwe amayankhulapo pa nkhani zosiyanasiyana mdziko muno a Dr George Chaima , ayamikira Mtsogoleri wa dziko lino  Dr Lazarus Chakwera […]

A baseline survey conducted by RBM in 2014 revealed that only 17% of adults utilized formal financial services, while a significant 53% relied on informal options. This gap is largely attributed to a lack of understanding of formal financial products, reflected in a concerning financial literacy index of just 3.6%. RBM Governor Wilson Banda emphasized […]

Sabata silimatha anthu okhala Mmizinda ndi mma town a Dziko lino asadaone zibinyira za zinyalala mphepete mwa Misewu zikudikira kunyamulidwa kuti zipite ku Mtaya. A Stephen Chiunjira ndi nkulu wa  Bungwe la Our World international ,yomwe imapanga zosintha zinyalala kuti zikhale Manyowa ndi zinthu zina zosiyanasiyana ku Kawale 2, mu Mzinda wa Lilongwe . Iwo […]

Kwa nthawi yaitali anthu mdziko muno akhala akututumuka ndi imfa zokudza  pongodzipha.A Joseph Maseke, katswiri pa nkhani yoona za thanzi la mmalingaliro watambasula kuti kaganizidwe ka ngwiro ndi kukhala osakhumudwa kapena nkhawa mmalingaliro. A Maseke atchula  ma ubwenzi amene achinyamata amakhala nawo kuti ali ndi kuthekera kwa kukulu kokhudza kaganizidwe ka ngwiro. Katswiri-yu wadandaula  kuti […]


Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist