Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist

Author: Kradio

Page: 3

Mukayenda mmakwalala,nzikhuthe ,malo ochitira ma sewero osiyanasiyana ndi kwina komwe achinyamata amasonkhana mupeza kuti pakati pawo pamakhala chikoka cha kugawana zakumwa ndi Fodya . Zambiri mwa izo  zimakhala Mankhwala ozunguza ubongo. Katswiri pa thanzi la kaganizidwe ka ngwiro a Joseph Maseke, ati Mankhwala ozunguza ubongo ndi Mankhwala omwe mkati mwake muli zinthu zosokoneza ubongo. “Pali […]

Mkhalakale pa Ndale a Jessey Kabwira ,apempha Bungwe lothana ndi Katangale ndi Ziphuphu la ACB,kuti lichitepo kanthu pofufuza ndi kupereka chilango kwa anthu omwe amachita katangale ponena kuti dzikoli likunyeka pa moto kaamba ka mchitidwe wu. Kabwira wati mdani wa mkulu wa utsogoleri wabwino ndi kudzikonda komwe kumachititsa kuti atsogeri azidzikundikira chuma. Utsogoleri umayenera kuimira […]

Pamene ngozi zagwa mwadzidzidzi anthu amakhala kakasi kusowa mtengo ogwira, izi ndi kutsatira kusakhala ndi ishulansi pa moyo wamunthu kapena katundu. Imodzi mwa bank yochita zinthu zake mwa makono ya Centenary, ili kalikiliki gugulitsa insurance kuti anthu asamatuluke thukuta zovuta zikaagwera. Mkulu oyanganira ntchito za Bank-assurance ku Centenary bank a James Akuseka Msiska , wati […]

Mneneri mu nthambi ya unduna wa zokopa alendo ndi zachirengedwe, a Joseph Nkosi ati dziko la Malawi likupita patsogolo potukula ntchito yosamalrira malo osungira Nyama za kutchire ndi zachirengedwe zomwe ziri ndi kuthekera kotukula dziko lino pa Chuma. Polankhula mu Program ya “Touring Malawi”  pa wailesi ya Kasupe , a Nkosi afotokoza kuti malo osungira […]

A renowned economic expert Mavuto Bamusi has raised serious concerns about Malawi’s mounting debt, which currently stands at a staggering 14 trillion kwacha. Bamusi criticized the government’s handling of the debt situation, urging for a strategic shift towards investing in more productive areas to stabilize the economy. He emphasized that without significant investments in productive sectors, […]

Tsiku silitha pasadachitike malonda aliwonse. A Zebron Lewis ochokera ku area 9 mu mzinda wa Lilongwe akhala akuchita geni. Bambo Lewis adayamba ndi geni yogulitsa Nyemba poyendanazo ku area 24, zaka zingapo zapitazo. Kuchulukana kwa anthu ogulitsa malondawa ku area 24,kudawapangitsa a Lewis kumakachitirageniyi ku area 25 ndi 49. Pakupita kwa nthawi nkuluyu adasintha mtundu […]

Mkhalakale pa Ndale a Jessey Kabwira ,apempha Bungwe lothana ndi Katangale ndi Ziphuphu la ACB,kuti lichitepo kanthu pofufuza ndi kupereka chilango kwa anthu omwe amachita katangale ponena kuti dzikoli likunyeka pa moto kaamba ka mchitidwe wu. Kabwira wati mdani wa mkulu wa utsogoleri wabwino ndi kudzikonda komwe kumachititsa kuti atsogeri azidzikundikira chuma. Utsogoleri umayenera kuimira […]

Boma la Malawi kudzera ku nthambi ya zachuma laonjola bank ya reserve ya mdziko mumo poipatsa ndalama zokwana 600 billion Malawi Kwacha kutsatira kuduka kwa bank yi ndi ndalama zokwana 539 billion Malawi. Katswiri pa nkhani zachuma a Greenson Nyirenda ,ati dziko lino siridafike pokhazikika pa chuma. Kuduka pa chuma kwa bank ya reserve kukutanthauza […]

Malonda ambiri mdziko muno amayamba akwezedwa pa Sikelo asanasinthanitsidwe ndi ndalama. Ndi Malonda amodzi okha a Golide omwe atati akwezedwa pa Sikelo atha kusinthanitsidwa ndi 150 Million Malawi Kwacha pa Kilogram imodzi.Miyala ya Mtengo wapatali ndiyo ili ndi kuthekera koonjola anthu pa umphawi wa dzaoneni. Malingana ndi kafukufuku dziko la Malawi ndi dziko losaukitsitsa kwambiri […]

Tsiku silitha pasadachitike malonda aliwonse. A Zebron Lewis ochokera ku area 9 mu mzinda wa Lilongwe akhala akuchita geni. Bambo Lewis adayamba ndi geni yogulitsa Nyemba poyendanazo ku area 24, zaka zingapo zapitazo. Kuchulukana kwa anthu ogulitsa malondawa ku area 24,kudawapangitsa a Lewis kumakachitira geniyi ku area 25 ndi 49. Pakupita kwa nthawi nkuluyu adasintha […]


Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist