Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist

Blog

Page: 2

Zamoyo zirizonse zimayenera kulandira chakudya cha bwino  kuti zidzikula ndi thanzi. Nayo mbewu ndi chimodzi mwa zinthu za Moyo zomwe zimafuna zakudya zabwino.A Tyson Chapuma, yemwe ndi Mlangizi pa nkhani za Ulimi ku Lunyangwa  research station  m’boma la Mzuzu , wati akugwira ntchito  usiku ndi usana kufufuza za chakudya cha mbewu mu nthaka. Pothirirapo mulomo […]

Next Level Academy, a renowned initiative from the United States of America , has praised Malawi for making significant strides in the creative arts industry. The sentiments were shared by MeccaGodZilla, the team leader for Next Level Academy, during a 10-day masterclass and workshop being held in Lilongwe. The workshop is designed to provide intensive […]

Nyimbo ndi chinthu chokhacho chimene chimathuzitsa mtima pamene munthu ali m’chisoni, kukuza chimwemwe kwa munthu amene ali mchisangalalo komanso kuthandizira kugwira ntchito  mosafooka. Gulu la Peace  Soldiers  , lomwe limayimba chamba cha Reggae, lati lidabadwa mu chaka cha 2003 ndi cholinga chofuna kupeza njira  pa  kulankhula pa zomwe gululi linkadana nazo ku Sukulu ya Secondary. […]

Pa zinthu zomwe munthu amaganizira tsiku ndi tsiku ndalama  imakhala pa mndandanda wa zinthu zoganiziridwa. Kaganizidwe kangwiro nako ndi kofunikira pa nkhani ya ndalama. Benard  ChiluzI, yemwe ndi Mkulu oyang’ana za maphunziro abwino a kayendetsedwe ka chuma ,wati kuganiza molungama ndi kaganizidwe komwe sikungamupezetse munthu mavuto kapena ndi kuganiza mu njira ina chifukwa cha zinthu […]

Litsiro ndi chinthu chokhacho chimene tsiku lake lobadwa silimadziwika ndipo limaberekana mwa kathithi. Mthupi mwa munthu namo mumakhala litsiro. Namkungwi pa nkhani ya zakudya,  Gladys Bandawe ,kuchokera ku Hope nutrition Services, watutumutsa mtundu wa a Malawi ponena kuti mthupi mwa munthu mumakhala litsiro.” Mkati mwathupi mumakhala litsiro limene limafunika kutsuka chimodzimodzi   limene limakhala kunja kwa […]

Pa miringo ya zinthu zomwe zimalingidwa pali mulingo umodzi wokha umene umapereka mafunso   ngati kalingidwe kakusemba ndondomeko maka olingayo akakhala wa mamuna ndipo akulinga munthu wa mkazi. Chovala , ndi chithu chokhacho chomwe chimalingidwa ndi mmisiri wosoka. Thomson Geza, Yemwe ndi mmodzi mwa wosoka zovala ku msika wa  Galliver mu mzinda wa Lilongwe, wavomereza kuti […]

Kusowa kwa maphunziro a za Chuma  pakati pa a Malawi  kuli ngati kusowa kwa  Chipatso cha Mpinjipinji Mnkhalango za dziko lino.Katswiri pa nkhani za Chuma a Innocent Banda, watsindika kuti ma Phunziro a za Chuma ndi osowa ngakhale ali ofunika. “Maphunziro a za chuma ndi ofunika chifukwa ndi chimene chimapereka mphamvu kwa anthu pothetsa umphawi,kutukula […]

Ndizosabisa kunena kuti Moto wa khala la Mtengo wa Tsanya omwe umayaka ku Bungwe lothana ndi Katangale ndi Ziphuphu  tsopano uli ngati Moto wa Mapesi. Katswiri woyankhulapo pa nkhani za Utsogoleri wabwino komanso momwe zinthu zikuyendera mdziko muno   Victor  Chipofya, wati sakumva nkhani  mma Nyuzipepala  ngati momwe zinaliri mbuyomu .”Sitikumva zinthu mma Nyuzipepala ngati mmene […]

Mdima wa ndiwe yani  wokhudza zomwe zidachitika kuti ndege yomwe idanyamula wachiwiri wa kale wa  Mtsogoleri wa dziko lino Malemu Dr Saulosi Klaus Chilima , udakakodolabe Mitsinje ya misonzi kwa a Mary Chilima ,omwe  pa 29 September 2024  adalemba pa tsamba la mchezo la facebook  kupempha  okhuzidwa onse kuti awathandize kupanga kafukufuku wapadera. Iwo adajambulitsa  […]

Mkuluwiko wokuti zingalume phula n’tenga ndi nkuluwiko omwe wamangirira  uthenga omwe Mtsogoleri wa dziko lino  Dr Lazalus Chakwera,  anali nawo kwa mamulumuzana a Bungwe la mgwirizano wa Maiko  apa dziko lonse lapansi. Mmodzi mwa akatswiri omwe amayankhulapo pa nkhani zosiyanasiyana mdziko muno a Dr George Chaima , ayamikira Mtsogoleri wa dziko lino  Dr Lazarus Chakwera […]


Kasupe Radio Live

Kasupe Radio Live

Current track

Title

Artist